nya-x-nyanja_gen_text_reg/47/23.txt

1 line
300 B
Plaintext

\v 23 Ndipo Yosefe anakamba kubantu kuti, " Onani, nagulila Farao imwe na malo yanu lelo. manje izi ni mbeu zanu, zamene muzashanga mu malo. \v 24 Pa kukolola, mufinika kupasa Farao zachisanu ndipo mbali fo zizankhala zanu, chifukwa mbeu za mumunda ndi za chakudya niza munyumba mwanu nabana banu."