nya-x-nyanja_gen_text_reg/47/20.txt

1 line
467 B
Plaintext

\v 20 Ndipo Yosefe anagulila malo yonse ya Igipito Farao. Pakuti muntu aliyese wamu Igipito anagulisa munda wake, chifukwa kunali njala yopitilila. Munjila iyi, malo anakhala ya Farao. \v 21 Kuli bantu, banakhala akapolo bake kuchokela kumalile ena ya Igipito kufika kumalile kosiliza. \v 22 Nimalo aba sombe chabe yamene Yosefe sanagule, chifukwa basembe anabapasa zobatandizila. Banadya zobangabila kuchokela kwa Farao zamene anabapasa. Mwaiche sanagulise malo yao.