nya-x-nyanja_gen_text_reg/47/07.txt

1 line
362 B
Plaintext

\v 7 Ndipo Yosefe analota Yakobo atate bake na baonesa kuli Farao. Yakobo anadalisa Farao. \v 8 Farao anauza Yakobo kuti, " Kodi wamkhala kwanthawi itali bwanji ?" \v 9 Yakobo anuza Farao, " zaka zakuyenda kwanga ni 130 zaka zamoyo wanga ni zing'ono ndipo zobaba. Sizambili ngati zamakolo banga banafa." \v 10 Ndipo Yakobo anadalisa Farao na kuchoka pameso yake.