nya-x-nyanja_gen_text_reg/46/28.txt

1 line
376 B
Plaintext

\v 28 Yakobo anatuma Yuda kuli Yosefe kuti amulangise njila yaku Gosheni, ndipo anabwela kumalo ya Gosheni. \v 29 Yosefe anakonza ngolo yake noyenda muku kumanya Israyeli atate bake kumalo ya Gosheni. Ana bawona, no kumbatila mu mukosi, ndipo analila pamukosi, pantawi yayitali. \v 30 Israyeli anauza Yosefe, "anje lekani nife, pakuti nawona pamenso pako, kuti ukachili moyo."