nya-x-nyanja_gen_text_reg/44/30.txt

1 line
455 B
Plaintext

\v 30 Apa, manaje, nikafika ku wanchito wanu atate, tilibe mung'ono wathu, chifukwa moyo wake wamangila pali muyo wa munyamata uyu. \v 31 Chizachitika akaona kuti tilibe munyamata ife azamwalila. Ba kapolo banu bazabwelasa imvi za kapolo wamu atate mu chisoni paka kumanda. \v 32 Chifukwa kapolo wanu ine ninakala chisimikizo ca munyamata kuli batate nokamba kuti, ngati sinza bwela nayeve, kuli imwe, apo nizankala wa milandi kwa atate banga tawi zonse.