nya-x-nyanja_gen_text_reg/43/32.txt

1 line
519 B
Plaintext

\v 32 Wachito ana konza chakudya cha Yosefe kwa eyeka ndipo abale bake pa beka aku Igoipito ano anadya pabeba chifukwa aku Igipito sanali dyele mukate pamozi nama Hebeli. Kwa ici ni chonyesa ku banthu ba ku Igipito. \v 33 Abale bake ana nkhala pamaso pake Oyamba kubadwa kukonka mwamene bana badwila. Ndipo wa cicepele kuligana na uyamata wake anthu ana dabwisiwa chapamozi. \v 34 Yosefe anatuma mupimo wazakudia pa songolo pake. Koma Benjamini mupimo unali usanu kupabana a bale ake. Anamwa ndipo bana kondwela na eve.