nya-x-nyanja_gen_text_reg/43/16.txt

1 line
265 B
Plaintext

\v 16 Pamene Yosefe anaona Benjamini pamozi ano, a na kamba kuli osungila nyumba yake." Ba lete banthu munyumba, paya nyama ndi mpika daba banthu bazadya na ine muzuba. \v 17 Osunga zamunyumba ya Yosefe ana chita monga Yosefe akambila. Anabaleta kunyumba ya Yosefe.