nya-x-nyanja_gen_text_reg/43/13.txt

1 line
408 B
Plaintext

\v 13 Tenganiso mubale wanu. Nyamuka ndi ku yendaso kwa munthu uyu. \v 14 Lekani mulungu wamphamvu zonse akupaseni imwe chifundo pamaso ya munthu uyu, kwakuti akamulekeleko mubale wanu ndi Benjamani gati nafielewa mwana, na feleawa. \v 15 Anthu anatenga paso izi. Ndi mu manja yao antenhga zopatikiza muyeso wa dalama, pamozi ndi Benjamini. Ana nysmuka ndi kuyenda pasi ku Igipito ndi ana imilila kwa Yosefe.