nya-x-nyanja_gen_text_reg/43/03.txt

1 line
348 B
Plaintext

\v 3 Yudu ana bauza eo. " Munthu monenesa anaticejeza ife. 'Simuza ona nkhope yanga kufikila mubale wanu ngati ali naimwe.' \v 4 Ndati muza tituma namubale wathu, tiza enda pasi ndi ku gulalila imwe vakudia. \v 5 Ngati simumutuma eve, citi zaenda pansi, daba uyu munthu anakamba kwaise, simuza ona nkhope yanga pokapo mubale wanu ngatiali naimwe.'"