nya-x-nyanja_gen_text_reg/36/37.txt

1 line
401 B
Plaintext

\v 37 Pamene Samlahi anafa, ndiye Shauli waku Rehoboth ku kamumana ana lamulila pa malo yake. \v 38 pamene Samlahi anafa,ndiye pamene Baal-Hanani mwana mwamuna wa Akbor, ndiye ana lamulila pa malo yake. \v 39 pamene Baal-Hanani mwana mwamuna wa Akbor, anafa, ndiye pamene Hadar ana lamulila pa malo yake. ZIna ya muzinda yake yenzeli Pau. Zina yamu kazi wake inali Mehetabeli mwana mukazi wa Me Zahab.