nya-x-nyanja_gen_text_reg/31/26.txt

1 line
367 B
Plaintext

\v 26 Ndipo Labani anakamba kuli Yakobo, wacita cani, kuti unani nama nakunyamula bana banga bakazi monga ba kaida ba nkhondo? \v 27 Cifukwa nicani unathaba mwacisinsi na kuninama ndiponso sunani uze ine? Asembe nina kupelekeza nakusangalala na nyimbo, ndi lingaka ndi coliza. \v 28 Sunandi vomekeze ine ku mpsompsona bana banga bakazi na bamuna, manje wacita vopusa.