nya-x-nyanja_gen_text_reg/31/19.txt

1 line
280 B
Plaintext

\v 19 Pamene Labani anayenda kukasenga nkhosa zake, Rakele anaba tumilungu twa munyuma ya batate bake. \v 20 Yakobo ana namanso Labani wa ku Aramean, po samu uza ati ayenda. \v 21 Ndipo anathaba na vonse enze navo na kudusa pa mumana, ndipo anayendela ku phili yaziko ku Giliyadi.