nya-x-nyanja_gen_text_reg/31/17.txt

1 line
281 B
Plaintext

\v 17 Ndipo Yakobo ananyamuka noika bana bake bamuna na bazikazi bake pa ma bulu. \v 18 Anaika zobeta zake pa songolo pake, pamozi nakatundu wake bonse, kuikilapo nanyama za mene anakhala nazo mu paddani Aramu. Ndipo anakonzekera kuyenda kuli Isaki tate wake mumalo yao ya Kanaani.