|
\v 4 Yacobo anatuma ndi kuitana Rakele ndi Leya kui abwele kumunda kuli zobeta zake. \v 5 Ndipo anakamba na beve, "Naona kayanganidwe kaba tate banu pali ine kacinja, koma Mulungu wa tate ali naine. \v 6 Muziba kuti na mpavu zanga zonse nankhala nisebenzela batate banu. |