nya-x-nyanja_gen_text_reg/30/14.txt

1 line
490 B
Plaintext

\v 14 Rubeni anayenda mu munda pa masiku yochosa witi nakupeza maudeleki mu munda. Anayabwelesa kuli mayi wake Leya. Pamene Recho anakamba kuli Leya, "Unipaseko maudeleki yenangu ya mwana wako mwamuna." \v 15 Leya anakamba kuli enve, "Iyi ninkani ing'ono kuli iwe? kuti unanipoka mwamuna wanga? Manje ufuna kunitengela na mandeleki ya mwana mwanga mwamuna?" Recho anakamba kuti ndiye pamene azagona naiwe usiku walelo, chifukwa cha mandeleki yamwana wako yamene uzani pasako mochinjanisha."