nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/28.txt

1 line
336 B
Plaintext

\v 28 Banamuyanka kuti zoona taona kuti Yehova alina iwe. Ndipo taganiza kuti pankale kulapila pakati patu pakati patu na iwe. Manje tiyeni tipange chipangano naiwe, \v 29 kuti silizatichita ise choipa, monga mwamene ise sitinaku chite voipa, monga mwamene tinakusungila bwino nakulaila mwa mutendele. Zoona, ndipo odalisika na Yehova."