nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/26.txt

1 line
225 B
Plaintext

\v 26 Ndipo Abimeleki anayenda kuli eve kuchokela ku Gerari, na Ahuzzati, na mu zake, na Phico, mukulu wa ba silikali. \v 27 Isaki anabauza, nichani mwabwelela kuli ine pakuti muni zonda ndipo muna nipisha kuchoka kuli imwe?"