nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/23.txt

1 line
395 B
Plaintext

\v 23 Kuchoka apo Isaki anachokako naku yenda ku Beereseba. \v 24 Yehova anamuokela usiku wamene uja nakukamba, "ndine Mulungu wa Abrahamu tate wako usayope, pakuti nili naiwe ndipo niza kudalisa iwe naku chulukisa bobadwa muli iwe chifukwa cha Abrahamu wa nchito wanga. \v 25 Isaki anamanga guwa kuja na kuitana pa ziko ya Yehova. Kuja ana kokomela hema, ndipo banchito bake bana kumba cisime.