nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/12.txt

1 line
299 B
Plaintext

\v 12 Isaki anashanga mbeu mu ziko muja naku kolola muchaka chamene kali handredi cifukwa Yehova anamudalisa. \v 13 Anankala mwamuna wolemela, ndipo anankala wolemela ndi kulemela paka anankala wolemela maningi. \v 14 Anali na mbelele na ng'ombe zambili nabanja ukulu. Ba Philistini bana mukumbwila.