nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/06.txt

1 line
421 B
Plaintext

\v 6 Ndipo Isaki anankala ku Gerari. \v 7 Pamene bazimuna bana funsa pali mukazi wake, anakamba. "Nimulongo wanga." ananvela mantha kukamba, "Nimu kazi wanga," chifukwa enzekuganiza, bazimuna bakuno ku malo bazani paya kuti batenge Rabeka, chifukwa niwabwino." \v 8 Pamene Isaki anakalako maningi kuja Abimelelki mfumu wabo ba Philistini ana sonjela pa (Zenela). Anayanga onani, Isaki anali ku gwila Rabeka, mukazi wake.