nya-x-nyanja_gen_text_reg/13/10.txt

1 line
365 B
Plaintext

\v 10 Ndipo Lote anayangana yangana nakuona kuti malo onse amanzi a Yolodani yanali yonyolowa bwino paliponse mpaka ku zowa, monga munda wa yawe, monga dothi ya ku Egypito. Apa nishi mulungu akalibe kuononga Sondomu na Gomola. \v 11 Apa Lote anazisankhila payeka malo akufupi namanzi yonse ku mumana wa Yolondono ndipo anyyenda chakumawa, ndipo abalewa anatayikana.