nya-x-nyanja_gen_text_reg/13/08.txt

1 line
339 B
Plaintext

\v 8 Abramu anakambisana na Lote, "pasankhala kuvutana pakati paiwe na ine, ndipo pakati pa sunga vinyama wako na wanga; ndawa, nipachibale apa. \v 9 Malo yonse siyowonekela kuli iwe pitiliza ndipo uzi choseko weka kuli ine. Ngati uzayenda kulefuti ine nizayenda kunangu. Kapena ngati uzayendala kukwanja kodyela, ine nizayenda kulefuti."