nya-x-nyanja_gen_text_reg/02/21.txt

1 line
433 B
Plaintext

\v 21 yehova Mulungu analengesa munthu kuti agone tulo tukulu ndipo mwamuna anagona. Yehova Mulungu anatenga mbambo imozi ya mwamuna naku valapo pa malo ya tupi pamene abatenga mbambo. \v 22 Na mbambo yamene Yehova Mulungu anatenga kuli mwamuna anapanga mukazi na kumubwelesa kuli mwamuna. \v 23 Mwamuna anakamba, "Manje apa, iyi ni bonzo yama bonzo yanga, na tupi ya tupi yanga. Azaitaniwwa mukazi chifukwa anachokela kuli mwamuna."