nya-x-nyanja_gen_text_reg/02/09.txt

1 line
285 B
Plaintext

\v 9 Kuchokela kudoti yapansi yehova Mulungu analengasa mutengo uli onse ku kula zo oneka ku menso ndipo za bwino kudya. kufakilamo na mutengo na mutenga wa kuziwa chabwino na choipa. \v 10 Mumana unachikela mu Eden kutila munda. Kuchikela apo unamabikana ndipo unankala mimana zili 4.