nya-x-nyanja_gen_text_reg/02/04.txt

1 line
420 B
Plaintext

\v 4 Izi ndizochitika zokhudza kumwamba ndi dziko lapansi pamene zinalengedwa, pa tsiku limene Yehova Mulungu anapanga dziko lapansi ndi zakumwamba. \v 5 Panalibe chitsamba chamtchire padziko lapansi, ngakhale chomera chamthengo sichinamera, pakuti Yehova Mulungu anali asanavumbitsire mvula padziko lapansi, ndipo panalibe munthu wolima nthaka. \v 6 Koma kunkakwera nkhungu yotuluka pansi nathirira dziko lonse lapansi.