nya-x-nyanja_gen_text_reg/01/16.txt

1 line
366 B
Plaintext

\v 16 Mulungu anapanga zo sanikila vili vikulu, Ikulu imozi ku lamulila muzuba, ndi ing,ono ku lamulila usiku. Anapanga anso nenyezi. \v 17 Mulyngu anaviyika mu mwamba kuti vizi pasa ku wala pa ziko, \v 18 ku lamulia muzuba ndi usiku, ndi ku patula ku wala kuli mudima. Mulungu anaona ati inli ya bwino. \v 19 Ndiye ku nali ku mazulo ndipo kuseni. siku ya nambala fo