nya-x-nyanja_gen_text_reg/01/09.txt

1 line
228 B
Plaintext

\v 9 Mulungu anakamba, "Lekhani manzi pansi yakhale pa malo yomozi, lekhani malo yo yuma ya aneke," Chi na nkhale mwamene. \v 10 Mulungu ana itena malo yo yuma "ziko." na yonse manzi anaitana "nyanja." anaona ati inali yabwino.