nya-x-nyanja_gen_text_reg/01/03.txt

1 line
241 B
Plaintext

\v 3 Mulungu nakamba, "lekani kuwale," ndipo kunawala. \v 4 Mulungu anaona kuti kuwala kunali bwino. Anapatula kuwala kucoka ku mudima. \v 5 Mulungu anapasa zina ya kuwala "muzuba," na mudima "usiku." Kwenze kumazulo na kuseni, siku yoyamba.