nya-x-nyanja_gen_text_reg/01/01.txt

1 line
219 B
Plaintext

\c 1 \v 1 Po yamba, Mulungu anapanga ku mwamba na ziko ya pansi. \v 2 Ziko inalibe maonekedwe yabwino ndipo yenzelibe vinthu vilivonse. Mudima unali pamwamba pa nyanja. Muzimu wa Mulungu unali kuyenda pamwamba pa manzi.