\v 13 Mulungu anakamba na Nowa, " Naona kuti yakwana nthuwi, kuti nicosepo munthu wonnse cifukwa calo cazola na ciwawa vicitika mwa iye, Zoonadi, Nizabaononga pamozi ndi ziko. \v 14 Koma kuli iwe upange chombo kucokela kuci mtengo ca kipulesi. Upange zipinda mu chombo ndi kuyanzikapo coletsa manzi kungena mkati na kunja. \v 15 Umu ndiye mwamena uzapangila: Kutalimpa kwa chombo ikale mikonoila 300, kufupika kwake mikono ili 50, ndikutalimpa mikono 30.