\v 23 Ndipo munakamba kuli banchito banu, koma chabe mu bwele na m'bela wanu wamung'ono simuzakaona pa menso panga futi. \v 24 Ndipo chanabwela kuti pamene tinaenda kuli banchito banu atate, tinoba ma ya abwana banga. \v 25 Atate batu banakamba yendani futi mukatigulile vakudia. \v 26 Ndipo tinakamba, "Sitinga yendeko khoma ngati,mubale wathu wamung'ono alina ife, Tiza endo, chifukwa chakuti sitizakwanisa kuona pamenso pa uja munthu. Koma chabe nufana wathu ankale naife.'