\v 3 Farao anakamba kwa abale bake, " Mugwila nchito bwanji?" Bana kamba kwa Farao, " Banchito banu ama onera mbelele, za makolo bantu." \v 4 Ndipo banakamba kuli Farao futi, " Ise tabwela monga alendo muno mumalo. Kulibe zodwesela nyama zabachito bananu, chifukwa kuli njala yopitilila mumalo ya Kenani. Sopano manje, napapata lolani banchito banu kukhale mumalo ya Gosheni."