\v 18 Aba banthu ba nacita manta chifukwa bana pelekewa kunyumba ya yosefe. ba na kamba, " Ni chifukwa cha dalama yamene ina bwezelewa muma saka tawi yoyamba tina ikiliwa mukati. Kuti ati sakile mupata motisuza ife. Kuti ati mage ise ndi kutitenga akapolo ndi a bulu. \v 19 Ana mufikila osunga nyumba ya Yosefe ndi ku kamba naye po lobela munyumba, \v 20 anati bwana, koyamba ku gula vakudia.