\v 9 Abimeleki ana muitana Isaki kuli eve ana muza, "Ona, Zoona nimukazi wako chifukwa nichani unakamba kuti nimu longo wako?" Isaki ana muza eve, "chifukwa nenze kuona monga wina angani paye kuti amu tenge." \v 10 Abimeleki anakamba, " Nichani ichi chamena wachita kuli ise? Cinali nichapafupi kuti umozo wabantu agone namukazi wako, ndipo sembe watiletela kuchimwa pali ise." \v 11 Ndipo Abimeleki anaba Chenjeza bonse bantu naku bauza, "Aliyense wamene azangwila uyu mwamuna olo mukazi wake zoona azapaiwa."