nya-x-nyanja_gen_text_reg/42/05.txt

1 line
257 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 5 Bana ba Israyeli banabwera kugura pakati kabaja banabwera, cifuka njala inali mu ziko ya Kanani. \v 6 Ndipo Yosefe anali bolamulila ziko. Ndipo anali kugulisa kubanthu bonse ba muziko. Abale bake ba Yosefe banafika nakubelama pansi na nkhope zao pansi.