2020-11-20 10:50:08 +00:00
|
|
|
\v 5 Ndipo Farao anakamba kuli Yosefe, kukamba kutii, " Atate bako na babale bako babwela kuli iwe. \v 6 Malo ya Igipito yali pamaso yanu. Khazikisa ba tate bako ndi babale bako malo kudela ya bwino, malo ya Gosheni ngati uziba bamuna boyenera pakati pao, ubafake otsogolela zobeta."
|