nya-x-nyanja_gen_text_reg/26/21.txt

1 line
309 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 21 Ndipo bana kumba cisime cinangu, ndipo bana yambana pali icho, futi, ndipo anachitana anachipasa zina "Sitina." \v 22 Anachoka kuja ndipo anakumba futi cinangu cisime, koma sibana yambana pali ici. ndipo anachitana Tehoboti, nakukamba kuti. "Manje Yehova ati pangila malo ise, ndipo tiza tukuka mu ziko.