nya-x-nyanja_gen_text_reg/47/13.txt

1 line
292 B
Plaintext
Raw Permalink Normal View History

\v 13 Manje kunalibe zakudya mu ziko monse: cifukwa njala yenze yopilila. Ziko ya Igipito, na Kanani anaonongeka cifukwa ca mvula osankhalako. \v 14 Yosefe anaunjika ndalama zonse zinali mu Igipito namu Kanani, mogulisa zakidya kubantu. Ndipo Yosefe anapeleka ndalama ku malo ya amfumu Falao.